Mic Mash, Siggy Kim - Andisamala lyrics

[Mic Mash, Siggy Kim - Andisamala lyrics]

Amadyetsa mbalame zosalima
Amalimbit'sa zonse zosakhwima
Moyo waulele anandipatsa ambiri ma hour
Ndilibe chifukwa chodandaulaso za mawa
Mavuto angalimbe, Hakuna Matata
I matter to my father andisamala
Dziko lingandinyoze, sindichita mantha
I’m never alone

I’ll never worship other gods like Aaron
Sawelengela phulupulu zanga
Zomwe ndimachita ndi anzanga
Ngakhale ndimachimwa mbuye wanga sanditaya
Ine ndikamaphwa iye amandipopa ngati tire
(Eeeeh Eeeh) you gave me life
I lift your name higher
(Eeeh eeeh) you the reason
Why ndikuimba ndi choir
Ndithange ufumu wanu zinthu zanu ndizakwaya
At the end of the day I
Don’t want to go to fire

Andisamala andisamala
Andisamala amasamala adzasamala
Andisamala andisamala
Andisamala amasamala adzasamala
Andisamala andisamala
Andisamala amasamala adzasamala

Feeding feeding is what you do
You give food to the poor and the need
Lord healing healing is what you do you heal
All the people who are sick in beds
Your the one who gives directions to them
Your the one who wipes away all the tears
I will worship you
I will always praise your name
Your the one who controls all the world

Andisamala andisamala
Andisamala amasamala adzasamala
Andisamala andisamala
Andisamala amasamala adzasamala
Andisamala andisamala
Andisamala amasamala adzasamala

Mudzasamala baba mudzasamala
Mumasamala oooh ooooh oooh oooouuh ooooh

Interpretation for


Add Interpretation

Add extended interpretation

If you know what the artist is talking about, can read between the lines, and know the history of the song, you can add interpretation to the lyrics. After checking by our editors, we will add it as the official interpretation of the song!

Latest added interpretations to lyrics

A B C D E F G H I J K L M N O P Q R S T U V W X Y Z #
Interpret